Hoseya 13:6 - Buku Lopatulika6 Monga mwa podyetsa pao, momwemo anakhuta; anakhuta, ndi mtima wao unakwezeka; chifukwa chake anandiiwala Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Monga mwa podyetsa pao, momwemo anakhuta; anakhuta, ndi mtima wao unakwezeka; chifukwa chake anandiiwala Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndidaŵadyetsa, nakhuta, koma atakhuta, adanyada, ndipo adandiiŵala Ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pamene ndinawadyetsa, iwo anakhuta; iwo atakhuta anayamba kunyada; ndipo anandiyiwala Ine. Onani mutuwo |