Hoseya 12:9 - Buku Lopatulika9 Koma Ine ndine Yehova Mulungu wako chichokere dziko la Ejipito, ndidzakukhalitsanso m'mahema, monga masiku a zikondwerero zoikika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma Ine ndine Yehova Mulungu wako chichokere dziko la Ejipito, ndidzakukhalitsanso m'mahema, monga masiku a zikondwerero zoikika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Koma Ine ndine Chauta, Mulungu wanu, amene ndidakutulutsani ku Ejipito. Ndidzakukhalitsaninso m'mahema, monga munkachitira masiku amakedzana m'chipululu muja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Ine ndine Yehova Mulungu wako amene ndinakutulutsa mu Igupto. Ndidzakukhazikaninso mʼmatenti, monga munkachitira masiku aja pa nthawi ya zikondwerero zanu. Onani mutuwo |