Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Hoseya 12:5 - Buku Lopatulika

5 ndiye Yehova Mulungu wa makamu, chikumbukiro chake ndi Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 ndiye Yehova Mulungu wa makamu, chikumbukiro chake ndi Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Ameneyu ndiye Chauta, Mulungu Wamphamvuzonse. Anthu azimkumbukira ndi dzina lakeli loti Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, Yehova ndiye dzina lake lotchuka!

Onani mutuwo Koperani




Hoseya 12:5
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Yakobo anauka m'tulo take, nati, Ndithu, Yehova ali mommuno; ndipo sindinadziwe.


Ndipo Yakobo anatcha dzina la malo amenewo, Penuwele: chifukwa ndaonana ndi Mulungu nkhope ndi nkhope, ndipo wapulumuka moyo wanga.


Ndipo Mulungu anamuonekeranso Yakobo, pamene iye anachokera mu Padanaramu, namdalitsa iye.


Dzina lanu, Yehova, likhala kosatha; chikumbukiro chanu, Yehova, kufikira mibadwomibadwo.


Imbirani Yehova, inu okondedwa ake, ndipo yamikani pokumbukira chiyero chake.


Ndipo Mulungu ananenanso kwa Mose, Ukatero ndi ana a Israele, Yehova Mulungu wa makolo anu, Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isaki, ndi Mulungu wa Yakobo anandituma kwa inu; ili ndi dzina langa nthawi yosatha, ichi ndi chikumbukiro changa m'mibadwomibadwo.


Ine ndine Yehova; dzina langa ndi lomweli; ndipo ulemerero wanga Ine sindidzapereka kwa wina, ngakhale kunditamanda kwa mafano osemedwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa