Hoseya 11:10 - Buku Lopatulika10 Adzatsata Yehova, Iye adzabangula ngati mkango; pamene abangula, ana adzafika ndi kunjenjemera kuchokera kumadzulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Adzatsata Yehova, Iye adzabangula ngati mkango; pamene abangula, ana adzafika ndi kunjenjemera kuchokera kumadzulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Ndidzaŵabangulira ngati mkango, ndipo anthu anga adzanditsata. Ndidzabanguladi, ndipo adzathamangira kwa Ine ali njenjenje kuchokera kuzambwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Iwo adzatsatira Yehova; Iye adzabangula ngati mkango. Akadzabangula, ana ake adzabwera akunjenjemera kuchokera kumadzulo. Onani mutuwo |