Hoseya 10:1 - Buku Lopatulika1 Israele ndi mpesa wotambalala, wodzibalira wokha zipatso; monga umo zinachulukira zipatso zake, momwemo anachulukitsa maguwa a nsembe ake; monga mwa kukoma kwake kwa dziko lake anapanga zoimiritsa zokoma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Israele ndi mpesa wotambalala, wodzibalira wokha zipatso; monga umo zinachulukira zipatso zake, momwemo anachulukitsa maguwa a nsembe ake; monga mwa kukoma kwake kwa dziko lake anapanga zoimiritsa zokoma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Aisraele ali ngati mpesa wokondwa umene unkabala zipatso zambiri. Chuma chao chikamanka chichuluka, chipembedzo chachikunja chinkakulirakuliranso. Dziko lao likamanka litukuka, iwo ankakometserakometsera mafano ao amene ankaŵapembedza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Israeli anali mpesa wotambalala; anabereka zipatso zambiri. Pamene zipatso zawo zinanka zichuluka, anawonjezera kumanga maguwa ansembe. Pamene dziko lake linkatukuka, anakongoletsa miyala yake yopatulika. Onani mutuwo |