Hagai 2:2 - Buku Lopatulika2 Unenetu kwa Zerubabele, mwana wa Sealatiele, chiwanga cha Yuda, ndi kwa Yoswa mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, ndi kwa otsala a anthu, kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Unenetu kwa Zerubabele, mwana wa Sealatiele, chiwanga cha Yuda, ndi kwa Yoswa mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, ndi kwa otsala a anthu, kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Uthengawu, wopita kwa Zerubabele mwana wa Salatiyele, bwanamkubwa wa ku Yuda, kwa Yoswa mwana wa Yehozadaki, ndiponso kwa ena onse, udati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Yankhula kwa Zerubabeli mwana wa Sealatieli, bwanamkubwa wa Yuda, kwa Yoswa mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, ndi kwa anthu onse otsala. Afunse kuti, Onani mutuwo |