Genesis 9:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo Hamu atate wake wa Kanani, anauona umaliseche wa atate wake, nauza abale ake awiri amene anali kunja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo Hamu atate wake wa Kanani, anauona umaliseche wa atate wake, nauza abale ake awiri amene anali kunja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Hamu, bambo wake wa Kanani, ataona kuti Nowa bambo wake ali maliseche, adapita nakauza abale ake aŵiri aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Hamu, abambo ake a Kanaani ataona kuti abambo ake ali maliseche anakawuza abale ake awiri aja omwe anali panja. Onani mutuwo |