Genesis 9:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo anayamba Nowa kukhala munthu wakulima nthaka, ndipo analima munda wampesa: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo anayamba Nowa kukhala munthu wakulima nthaka, ndipo analima munda wamphesa: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Nowa anali mlimi ndipo anali woyamba kulima munda wamphesa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Nowa anali munthu woyamba kulima munda wamphesa. Onani mutuwo |