Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 9:20 - Buku Lopatulika

20 Ndipo anayamba Nowa kukhala munthu wakulima nthaka, ndipo analima munda wampesa:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndipo anayamba Nowa kukhala munthu wakulima nthaka, ndipo analima munda wamphesa:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Nowa anali mlimi ndipo anali woyamba kulima munda wamphesa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Nowa anali munthu woyamba kulima munda wamphesa.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 9:20
15 Mawu Ofanana  

Yehova Mulungu anamtulutsa iye m'munda wa Edeni, kuti alime nthaka m'mene anamtenga iye.


Ndipo anabalanso mphwake Abele. Abele anakhala mbusa wa nkhosa, koma Kaini anali wakulima nthaka.


namutcha dzina lake Nowa, ndi kuti, Yemweyu adzatonthoza mtima wathu pantchito zathu zovuta za manja athu, chifukwa cha nthaka imene anaitemberera Yehova;


Amenewa ndiwo ana aamuna atatu a Nowa: ndiwo anafalikira dziko lonse lapansi.


namwa vinyo wake, naledzera; ndipo anali wamaliseche m'kati mwa hema wake.


M'kamwa mwa wolungama ndi kasupe wa moyo; koma m'kamwa mwa oipa mubisa chiwawa.


Zakudya zikwanira wolima minda yake; koma wotsata anthu opanda pake asowa nzeru.


Ndinapita pamunda wa waulesi, polima mphesa munthu wosowa nzeru.


Phindutu la dziko lipindulira onse; ngakhale mfumu munda umthandiza;


Musayang'ane pa ine, pakuti ndada, pakuti dzuwa landidetsa. Ana aamuna a amai anandikwiyira, anandisungitsa minda yamipesa; koma munda wangawanga wamipesa sindinausunge.


Msilikali ndani achita nkhondo, nthawi iliyonse, nadzifunira zake yekha? Aoka mipesa ndani, osadya chipatso chake? Kapena aweta gulu ndani, osadya mkaka wake wa gululo? Kodi ndilankhula izi monga mwa anthu?


Ndipo ndani munthuyo anaoka munda wampesa osalawa zipatso zake? Amuke nabwerere kunyumba yake, kuti angafe kunkhondo, nangalawe munthu wina zipatso zake.


Mudzapalana ubwenzi ndi mkazi, koma mwamuna wina adzagona naye; mudzamanga nyumba, osakhala m'mwemo; mudzaoka munda wampesa, osalawa zipatso zake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa