Genesis 8:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo anatulutsa njiwa imchokere, kuti aone kapena madzi anaphwa pamwamba padziko lapansi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo anatulutsa njiwa imchokere, kuti aone kapena madzi anaphwa pamwamba pa dziko lapansi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsono Nowa adatulutsa nkhunda kuti ikaone ngati madzi aphwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Kenaka anatulutsa nkhunda kuti aone ngati madzi aphwa pa dziko. Onani mutuwo |