Genesis 8:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo anatuluka Nowa ndi ana ake, ndi mkazi wake, ndi akazi a ana ake, pamodzi naye: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo anatuluka Nowa ndi ana ake, ndi mkazi wake, ndi akazi a ana ake, pamodzi naye: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Motero Nowa adatuluka m'chombo, iye ndi mkazi wake ndiponso ana ake ndi akazi ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Nowa anatuluka pamodzi ndi ana ake aamuna, mkazi wake ndi akazi a ana ake. Onani mutuwo |