Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 8:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo anatuluka Nowa ndi ana ake, ndi mkazi wake, ndi akazi a ana ake, pamodzi naye:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo anatuluka Nowa ndi ana ake, ndi mkazi wake, ndi akazi a ana ake, pamodzi naye:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Motero Nowa adatuluka m'chombo, iye ndi mkazi wake ndiponso ana ake ndi akazi ao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Nowa anatuluka pamodzi ndi ana ake aamuna, mkazi wake ndi akazi a ana ake.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 8:18
5 Mawu Ofanana  

Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali padziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa padziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.


Tulutsa pamodzi ndi iwe zamoyo zonse zili ndi iwe za nyama zonse, zouluka, ndi zinyama, ndi zokwawa zonse zakukwawa padziko lapansi; kuti ziswane padziko lapansi, zibalane, zichuluke padziko lapansi.


zinyama zonse, zokwawa zonse, zouluka zonse, ndi zonse zokwawa padziko lapansi, monga mwa mitundu yao, zinatuluka m'chingalawamo.


Yehova adzasungira kutuluka kwako ndi kulowa kwako, kuyambira tsopano kufikira nthawi zonse.


imene inakhala yosamvera kale, pamene kuleza mtima kwa Mulungu kunalindira, m'masiku a Nowa, pokhala m'kukonzeka chingalawa, m'menemo owerengeka, ndiwo amoyo asanu ndi atatu, anapulumutsidwa mwa madzi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa