Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 8:14 - Buku Lopatulika

14 Mwezi wachiwiri tsiku la makumi awiri kudza asanu ndi awiri la mwezi, lidauma dziko lapansi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Mwezi wachiwiri tsiku la makumi awiri kudza asanu ndi awiri la mwezi, lidauma dziko lapansi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Pa tsiku la 27 mwezi wachiŵiri, dziko lonse lapansi linali litauma kotheratu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Pokwana tsiku la 27 la mwezi wachiwiri dziko lapansi linawumiratu.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 8:14
6 Mawu Ofanana  

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.


Ndipo panali chaka cha mazana asanu ndi limodzi kudza chimodzi, mwezi woyamba, tsiku loyamba mwezi, madzi anaphwa padziko lapansi; ndipo Nowa anachotsa tsindwi lake pachingalawa, nayang'ana, ndipo taonani, padauma padziko lapansi.


Mulungu ndipo ananena kwa Nowa, kuti,


Ndipo kunali chaka cha makumi atatu mphambu zisanu ndi ziwiri cha kumtenga ndende Yehoyakini mfumu ya Yuda, mwezi wakhumi ndi ziwiri, tsiku la makumi awiri mphambu asanu ndi awiri la mwezi, Evili-Merodaki mfumu ya Babiloni anamuweramutsa mutu wake wa Yehoyakini mfumu ya Yuda atuluke m'kaidi, chaka cholowa iye ufumu wake;


Ndipo kunali chaka cha makumi awiri mphambu zisanu ndi ziwiri mwezi woyamba, tsiku loyamba la mwezi, anandidzera mau a Yehova, akuti,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa