Genesis 7:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo panali pamene anapita masiku asanu ndi awiri, madzi a chigumula anali padziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo panali pamene anapita masiku asanu ndi awiri, madzi a chigumula anali pa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Patangopita masiku asanu ndi aŵiri, chigumula chidafika pa dziko lonse lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Patapita masiku asanu ndi awiri chigumula chinabwera pa dziko lapansi. Onani mutuwo |