Genesis 6:17 - Buku Lopatulika17 Ndine, taonani, ndipo Ine ndidzadzetsa chigumula cha madzi padziko lapansi, kuti chiononge zamoyo zonse, m'mene muli mpweya wa moyo pansi pathambo; zinthu zonse za m'dziko lapansi zidzafa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndine, taonani, ndipo Ine ndidzadzetsa chigumula cha madzi pa dziko lapansi, kuti chiononge zamoyo zonse, m'mene muli mpweya wa moyo pansi pa thambo; zinthu zonse za m'dziko lapansi zidzafa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ndidzagwetsa mvula yachigumula pa dziko lapansi, kuti iwononge zamoyo zonse. Zonse zapadziko zidzafa, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ndidzagwetsa mvula ya chigumula pa dziko lapansi kuti ndiwononge zamoyo zonse za pansi pa thambo ndipo chilichonse cha pa dziko lapansi chidzafa. Onani mutuwo |