Genesis 6:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Mulungu anaona dziko lapansi, ndipo taonani, linavunda; pakuti anthu onse anavunditsa njira yao padziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Mulungu anaona dziko lapansi, ndipo taonani, linavunda; pakuti anthu onse anavunditsa njira yao pa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Mulungu atayang'ana dziko lapansi, adaona kuti ndi lonyansa, chifukwa anthu onse anali oipa kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Mulungu atayangʼana, anaona kuti dziko layipadi chifukwa cha makhalidwe oyipa a anthu onse pa dziko lapansi. Onani mutuwo |