Genesis 6:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo dziko lapansi linavunda pamaso pa Mulungu, dziko lapansi ndipo linadzala ndi chiwawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo dziko lapansi linavunda pamaso pa Mulungu, dziko lapansi ndipo linadzala ndi chiwawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Koma anthu ena onse anali oipa pamaso pa Mulungu, ndipo kuipa kwao kudawanda ponseponse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Chiwawa chinadzaza pa dziko lapansi kotero kuti dziko linakhala lowonongeka pamaso pa Mulungu. Onani mutuwo |