Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 6:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo Nowa anabala ana aamuna atatu: Semu, Hamu ndi Yafeti.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo Nowa anabala ana amuna atatu, Semu, Hamu ndi Yafeti.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Anali ndi ana aamuna atatu: Semu, Hamu ndi Yafeti.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Nowa anabereka ana aamuna atatu: Semu, Hamu ndi Yafeti.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 6:10
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Nowa anali wa zaka mazana asanu; ndipo Nowa anabala Semu ndi Hamu ndi Yafeti.


Ndipo dziko lapansi linavunda pamaso pa Mulungu, dziko lapansi ndipo linadzala ndi chiwawa.


Mibadwo ya Nowa ndi iyi: Nowa anali munthu wolungama ndi wangwiro m'mibadwo yake; Nowa anayendabe ndi Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa