Genesis 50:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo tsopano musaope; ine ndidzachereza inu, ndi ana anu aang'ono. Ndipo anawatonthoza iwo mitima yao, nanena nao mokoma mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo tsopano musaope; ine ndidzachereza inu, ndi ana anu ang'ono. Ndipo anawatonthoza iwo mitima yao, nanena nao mokoma mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Tsopano inu musade nkhaŵa. Ndidzakusamalani pamodzi ndi ana anu omwe.” Motero adaŵalimbitsa mtima naŵasangulutsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Kotero, musachite mantha. Ine ndidzasamalira inu pamodzi ndi ana anu omwe.” Tsono iye anawalimbitsa mtima powayankhula moleza mtima. Onani mutuwo |