Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 50:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo anatumiza mthenga kwa Yosefe kuti, Atate wathu asanafe analamulira, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo anatumiza mthenga kwa Yosefe kuti, Atate wathu asanafe analamulira, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Motero adatumiza mau kwa Yosefe kuti, “Atate anu asanafe adanena mau akuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Motero anatumiza mawu kwa Yosefe kuti, “Abambo anu anasiya malangizo asanafe nati:

Onani mutuwo Koperani




Genesis 50:16
3 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene abale ake a Yosefe anaona kuti atate wao anafa, anati, Kapena Yosefe adzatida ife, ndipo adzatibwezera ife zoipa zonse tidamchitira iye.


Muziti chotero kwa Yosefe, Mukhululukiretu tsopano kulakwa kwa abale anu, ndi kuchimwa kwao, chifukwa kuti anakuchitirani inu choipa; tsopano mutikhululukiretu kulakwa kwa akapolo a Mulungu wa atate wanu. Ndipo Yosefe analira pamene iwo ananena ndi iye.


Kuopa anthu kutchera msampha; koma wokhulupirira Yehova adzapulumuka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa