Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 5:30 - Buku Lopatulika

30 ndipo Lameki anakhala ndi moyo atabala Nowa, zaka mazana asanu kudza makumi asanu ndi anai ndi zisanu, nabala ana aamuna ndi aakazi:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 ndipo Lameki anakhala ndi moyo atabala Nowa, zaka mazana asanu kudza makumi asanu ndi anai ndi zisanu, nabala ana aamuna ndi aakazi:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Lameki adakhalanso ndi moyo zaka zina 595. Adaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Atabadwa Nowa, Lameki anakhala zaka zina 595 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 5:30
3 Mawu Ofanana  

namutcha dzina lake Nowa, ndi kuti, Yemweyu adzatonthoza mtima wathu pantchito zathu zovuta za manja athu, chifukwa cha nthaka imene anaitemberera Yehova;


masiku ake onse a Lameki anali zaka mazana asanu ndi awiri kudza makumi asanu ndi awiri; ndipo anamwalira.


Masiku ake Adamu atabala Seti, anali zaka mazana asanu ndi atatu; ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa