Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 5:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo Kenani anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi awiri, ndipo anabala Mahalalele:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo Kenani anakhala ndi moyo zaka makumi asanu ndi awiri, ndipo anabala Mahalalele:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Kenani ali wa zaka 70, adabereka mwana dzina lake Mahalalele,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Pamene Kenani anali ndi zaka 70, anabereka Mahalaleli.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 5:12
3 Mawu Ofanana  

Masiku ake onse a Enosi anali mazana asanu ndi anai kudza zisanu; ndipo anamwalira.


ndipo Kenani anakhala ndi moyo, atabala Mahalalele zaka mazana asanu ndi atatu kudza makumi anai, ndipo anabala ana aamuna ndi aakazi;


mwana wa Metusela, mwana wa Enoki, mwana wa Yaredi, mwana wa Mahalalele, mwana wa Kainani,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa