Genesis 49:5 - Buku Lopatulika5 Simeoni ndi Levi ndiwo abale; zida za mphulupulu ndizo malupanga ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Simeoni ndi Levi ndiwo abale; zida za mphulupulu ndizo malupanga ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 “Simeoni ndi Levi mpachibale pao, amagwiritsa ntchito zida zankhondo pochita chiwawa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 “Simeoni ndi Levi ndi pachibale pawo, anachitira nkhanza anthu amene anachita nawo pangano. Onani mutuwo |