Genesis 47:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo Yakobo anamdalitsa Farao, natuluka pamaso pa Farao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo Yakobo anamdalitsa Farao, natuluka pamaso pa Farao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndipo atadalitsa Farao, adatsazikana naye nkuchokapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Atatha kumudalitsa Farao uja, Yakobo anatsanzika nʼkunyamuka. Onani mutuwo |