Genesis 46:3 - Buku Lopatulika3 Nati iye, Ndine pano. Ndipo anati, Ine ndine Mulungu, Mulungu wa atate wako; usaope kunka ku Ejipito; pakuti pamenepo ndidzakusandutsa iwe mtundu waukulu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Nati iye, Ndine pano. Ndipo anati, Ine ndine Mulungu, Mulungu wa atate wako; usaope kunka ku Ejipito; pakuti pamenepo ndidzakusandutsa iwe mtundu waukulu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndipo adamuuza kuti “Ine ndine Mulungu, Mulungu wa atate ako. Usaope kupita ku Ejipito. Kumeneko ndidzachulukitsa zidzukulu zako, kuti zikhale mtundu waukulu wa anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mulungu anati, “Ine ndine Mulungu. Mulungu wa abambo ako. Usachite mantha kupita ku Igupto, pakuti ndidzachulukitsa zidzukulu zako kumeneko moti zidzakhala mtundu waukulu. Onani mutuwo |