Genesis 45:6 - Buku Lopatulika6 Zaka ziwirizi muli njala m'dziko muno; ndipo zatsala zaka zisanu, zopanda kulima kapena kusenga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Zaka ziwirizi muli njala m'dziko muno; ndipo zatsala zaka zisanu, zopanda kulima kapena kusenga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Chaka chino ndi chaka chachiŵiri cha njala. Koma zakhalabe zaka zisanu, ndipo pa zaka zimenezi anthu sadzalima kapena kukolola. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kwa zaka ziwiri tsopano, kwakhala kuli njala mʼdziko muno, ndipo kwa zaka zisanu zikubwerazi, anthu sadzalima kapena kukolola. Onani mutuwo |