Genesis 44:3 - Buku Lopatulika3 Pamene kudacha, anamukitsa anthu iwo ndi abulu ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pamene kudacha, anamukitsa anthu iwo ndi abulu ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 M'maŵa kutacha, anthu aja adaloledwa kupita pamodzi ndi abulu ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mmawa kutacha anthu aja analoledwa kuti apite ndi abulu awo. Onani mutuwo |