Genesis 43:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Israele anati, Chifukwa ninji munandichitira ine choipa chotero kuti munamuuza munthuyo muli ndi mphwanu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Israele anati, Chifukwa ninji munandichitira ine choipa chotero kuti munamuuza munthuyo muli ndi mphwanu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Apo Israele adati, “Chifukwa chiyani mudathinitsa zinthu pa ine pomuuza kuti muli ndi mbale wanu winanso?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Tsono Israeli anafunsa kuti, “Bwanji inu munandiputira mavuto oterewa pomuwuza munthuyo kuti muli ndi mʼbale wanu wina?” Onani mutuwo |