Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 43:13 - Buku Lopatulika

13 mutengenso mphwanu, nimunyamuke, mupitenso kwa munthu uja:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 mutengenso mphwanu, nimunyamuke, mupitenso kwa munthu uja:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Mtengeni mbale wanuyu, ndipo nyamukani, mupitenso kwa munthuyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Mutengeninso mngʼono wanuyu ndi kubwerera kwa munthuyo msanga.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 43:13
3 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anati, Mwana wanga sadzatsikira ndi inu, chifukwa kuti mkulu wake wafa, ndipo watsala iye yekha; ngati choipa chikamgwera iye m'njira m'mene mupitamo, inu mudzatsitsira ndi chisoni imvi zanga kumanda.


nimutenge ndalama zowirikiza m'manja mwanu; ndipo ndalama zimene zinabwezedwa kukamwa kwa matumba anu mutengenso m'manja mwanu; kapena sanachite dala;


Mulungu Wamphamvuyonse adzakupatsani inu chifundo pamaso pa munthu uja, kuti akumasulireni inu mbale wanu wina ndi Benjamini. Ndipo ine, ngati ndikhala wopanda ana, ndikhalatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa