Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 42:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo anaika onse m'kaidi masiku atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo anaika onse m'kaidi masiku atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Atanena mau ameneŵa, adakaŵatsekera m'ndende masiku atatu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Ndipo onse anawayika mʼndende kwa masiku atatu.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 42:17
9 Mawu Ofanana  

Ndipo kazembe wa alonda anapereka iwo kwa Yosefe, ndipo iye anawatumikira iwo: ndipo anakhala nthawi mosungidwamo.


Ndipo anafunsa akulu a Farao osungidwa naye m'nyumba ya mbuyake, kuti, Nkhope zanu zagwa bwanji lero?


Farao anakwiya ndi anyamata ake, nandiika ine ndisungidwe m'nyumba ya kazembe wa alonda, ine ndi wophika mkate wamkulu:


Munachitira mtumiki wanu chokoma, Yehova, monga mwa mau anu.


Ndipo iwo adzasonkhanitsidwa pamodzi, monga ndende zimasonkhanitsidwa m'dzenje, ndi kutsekeredwa m'kaidi, ndipo atapita masiku ambiri adzawazonda.


Ndipo anamsunga m'kaidi, kuti awafotokozere m'mene anenere Yehova.


Ndipo anawathira manja, nawaika m'ndende kufikira m'mawa; pakuti mpa madzulo pamenepo.


nathira manja atumwi, nawaika m'ndende ya anthu wamba.


Pakutitu iwo anatilanga masiku owerengeka monga kudawakomera; koma Iye atero, kukatipindulitsa, kuti tikalandirane nao pa chiyero chake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa