Genesis 42:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo iwo anati kwa iye, Iai, mbuyanga, koma akapolo anu adzera kudzagula chakudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo iwo anati kwa iye, Iai, mbuyanga, koma akapolo anu adzera kudzagula chakudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Iwo aja adayankha kuti, “Iyai mbuyathu, ife atumiki anu tabwera kuti tidzagule chakudya basi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Iwo anayankha, “Ayi mbuye wathu, antchito anufe tabwera kudzagula chakudya. Onani mutuwo |