Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 41:9 - Buku Lopatulika

9 Pamenepo wopereka chikho wamkulu anati kwa Farao, kuti, Ine ndidzakumbukira zochimwa zanga lero.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Pamenepo wopereka chikho wamkulu anati kwa Farao, kuti, Ine ndidzakumbukira zochimwa zanga lero.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Pomwepo woperekera vinyo uja adauza Farao kuti, “Lero ndiwulule kulakwa kwanga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ndipo mkulu wa operekera zakumwa anati kwa Farao, “Lero ndakumbukira kulephera kwanga.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 41:9
4 Mawu Ofanana  

Koma undikumbukire ine m'mene kudzakhala bwino ndi iwe, ndipo undichitiretu ine kukoma mtima: nunditchule ine kwa Farao, nunditulutse ine m'nyumbamu:


Koma wopereka chikho wamkulu sanakumbukire Yosefe, koma anamuiwala.


kufikira nyengo yakuchitika maneno ake; mau a Yehova anamuyesa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa