Genesis 41:57 - Buku Lopatulika57 Ndipo maiko onse anafika ku Ejipito kudzagula tirigu kwa Yosefe: chifukwa njala inakula m'dziko lonse lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201457 Ndipo maiko onse anafika ku Ejipito kudzagula tirigu kwa Yosefe: chifukwa njala inakula m'dziko lonse lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa57 Anthu ankafika ku Ejipito kuchokera ku mbali zonse za dziko lapansi, kudzagula tirigu kwa Yosefe, chifukwa njala inali itakula koopsa konsekonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero57 Anthu ankabwera ku Igupto kuchokera ku mayiko ena onse kudzagula tirigu kwa Yosefe, chifukwa njala inafika poyipa kwambiri pa dziko lonse lapansi. Onani mutuwo |