Genesis 41:40 - Buku Lopatulika40 Uziyang'anira pa nyumba yanga, ndipo anthu anga onse adzalamulidwa mwa mau ako; pa mpando wachifumu pokha ine ndidzakuposa iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Uziyang'anira pa nyumba yanga, ndipo anthu anga onse adzalamulidwa mwa mau ako; pa mpando wachifumu pokha ine ndidzakuposa iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Iwe ndiwe amene udzalamulira dziko langa, ndipo anthu anga onse adzakumvera. Ine ndidzakupambana pa chokhachi choti ndine mfumu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Iwe ukhala nduna yayikulu mu dziko langa ndipo anthu onse adzamvera zimene walamula. Ine ndekha ndiye amene ndidzakuposa mphamvu chifukwa ndimakhala pa mpando waufumu.” Onani mutuwo |