Genesis 41:38 - Buku Lopatulika38 Ndipo Farao anati kwa anyamata ake, Kodi ife tidzaone munthu ngati uyu, mzimu wa Mulungu uli m'mtima mwake? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Ndipo Farao anati kwa anyamata ake, Kodi ife tidzaone munthu ngati uyu, mzimu wa Mulungu uli m'mtima mwake? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Tsono Farao adafunsa nduna zakezo kuti, “Kodi tingampeze kuti munthu wina woposa uyu amene ali ndi mzimu wa Mulungu?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Choncho Farao anafunsa nduna zake nati, “Kodi tingathe kumupeza munthu wina ngati uyu, amene ali ndi mzimu wa Mulungu?” Onani mutuwo |