Genesis 40:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Farao anakwiyira akulu ake awiriwo wamkulu wa opereka chikho, ndi wamkulu wa ophika mkate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Farao anakwiyira akulu ake awiriwo wamkulu wa opereka chikho, ndi wamkulu wa ophika mkate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Farao adaŵakwiyira kwambiri antchito ake aŵiriwo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Farao anapsa mtima ndi akuluakulu awiriwa, Onani mutuwo |