Genesis 40:17 - Buku Lopatulika17 m'lichero lapamwamba munali mikate ya Farao ya mitundumitundu; ndipo mbalame zinadya ya m'lichero la pamutu panga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 m'lichero lapamwamba munali mikate ya Farao ya mitundumitundu; ndipo mbalame zinadya ya m'lichero la pamutu panga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 M'nsengwa yapamwamba munali mitundu yambiri ya chakudya cha Farao, koma mbalame zinalikudya chakudyacho.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Mu nsengwa yapamwamba munali zakudya zamitundumitundu za Farao, koma mbalame zimadya zakudyazo.” Onani mutuwo |