Genesis 4:5 - Buku Lopatulika5 koma sanayang'anire Kaini ndi nsembe yake. Kaini ndipo anakwiya kwambiri, ndipo nkhope yake inagwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 koma sanayang'anire Kaini ndi nsembe yake. Kaini ndipo anakwiya kwambiri, niigwa nkhope yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma Kaini Chauta sadakondwere naye ndipo sadalandire chopereka chake. Chifukwa cha zimenezi, Kainiyo adakwiya kwambiri, kotero kuti nkhope yake inali yakugwa ndi yamasinya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Koma sanakondwere ndi Kaini ndi nsembe yake. Kotero Kaini anakwiya kwambiri ndipo nkhope yake inagwa. Onani mutuwo |