Genesis 4:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo Lameki anadzitengera yekha akazi awiri: dzina lake la wina ndi Ada, dzina lake la mnzake ndi Zila. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo Lameki anadzitengera yekha akazi awiri: dzina lake la wina ndi Ada, dzina lake la mnzake ndi Zila. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Lameki adakwatira akazi aŵiri. Dzina la mkazi wake woyamba linali Ada, la mkazi wachiŵiri linali Zila. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Lameki anakwatira akazi awiri, wina dzina lake linali Ada ndi winayo dzina lake linali Zila. Onani mutuwo |