Genesis 39:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo mbuyake anaona kuti Yehova anali ndi iye, ndi kuti Yehova anamlemereza m'dzanja lake zonse anazichita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo mbuyake anaona kuti Yehova anali ndi iye, ndi kuti Yehova anamlemereza m'dzanja lake zonse anazichita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Bwana wakeyo adaona kuti Chauta anali naye Yosefe, ndi kuti ankamukhozetsa pa zonse zimene ankachita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mbuye wake anaona kuti Yehova anali naye Yosefe ndi kuti pa chilichonse chimene anachita Yehova ankaonetsetsa kuti achite bwino. Onani mutuwo |