Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 39:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo panali pamene mkazi anaona kuti anasiya chofunda chake m'dzanja lake, nathawira kubwalo,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo panali pamene mkazi anaona kuti anasiya chofunda chake m'dzanja lake, nathawira kubwalo,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Tsono mkazi uja ataona kuti Yosefe wasiya mwinjiro ndipo wathaŵira pabwalo,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Pamene mkazi uja anaona kuti Yosefe wamusiyira mkanjo wake mʼmanja mwake nathawira kunja kwa nyumba,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 39:13
2 Mawu Ofanana  

Ndipo mkazi anagwira iye chofunda chake, nati, Gona ndi ine; ndipo anasiya chofunda chake m'dzanja lake nathawa, natulukira kubwalo.


anaitana aamuna a m'nyumba yake, nanena ndi iwo kuti, Taonani, walowetsa kwa ife Muhebri kuti atiseke ife, analowa kwa ine kugona ndi ine, ndipo ndinafuula ndi mau aakulu:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa