Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 38:28 - Buku Lopatulika

28 Ndipo panali pamene anabala kuti mmodzi anatulutsa dzanja; ndipo namwino anatenga chingwe chofiira namanga padzanja lake, kuti, Uyu anayamba kubadwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Ndipo panali pamene anabala kuti mmodzi anatulutsa dzanja; ndipo namwino anatenga chingwe chofiira namanga pa dzanja lake, kuti, Uyu anayamba kubadwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Pa nthaŵi yochira, mmodzi mwa anawo adatulutsa dzanja. Mzamba adaligwira, nalimanga ndi chingwe chofiira nati, “Ameneyu ndiye woyamba kubadwa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Pamene ankabereka, mmodzi wa iwo anatulutsa dzanja lake. Choncho mzamba anatenga kawulusi kofiira nakamangirira pa mkono pa mwanayo nati, “Uyu ndiye anayamba kubadwa.”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 38:28
3 Mawu Ofanana  

Pambuyo pake ndipo anabadwa mphwake ndipo dzanja lake linagwira chitendeni cha Esau, ndi dzina lake linatchedwa Yakobo: ndipo Isaki anali wa zaka makumi asanu ndi limodzi pamene mkazi wake anabala iwo.


Ndipo panali nthawi ya kubala kwake, taonani, amapasa anali m'mimba mwake.


Ndipo panali pamene iye anabweza dzanja lake, kuti, taona, mbale wake anabadwa, ndipo namwino anati, Wadziphothyolera wekha bwanji? Chifukwa chake dzina lake linatchedwa Perezi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa