Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 38:27 - Buku Lopatulika

27 Ndipo panali nthawi ya kubala kwake, taonani, amapasa anali m'mimba mwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndipo panali nthawi ya kubala kwake, taonani, amapasa anali m'mimba mwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Itakwana nthaŵi yakuti Tamara achire, m'mimba mwake munali mapasa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Pamene Tamara nthawi inamukwanira yoti abeleke, mʼmimbamo munali mapasa.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 38:27
2 Mawu Ofanana  

Atatha masiku ake akubala, taonani, amapasa anali m'mimba mwake.


Ndipo panali pamene anabala kuti mmodzi anatulutsa dzanja; ndipo namwino anatenga chingwe chofiira namanga padzanja lake, kuti, Uyu anayamba kubadwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa