Genesis 38:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo panali itapita miyezi itatu, anamuuza Yuda kuti, Tamara mpongozi wako wachita chigololo, ndiponso taonani, ali ndi pakati ndi chigololocho. Ndipo Yuda anati, Mtulutse iye kuti amponye pamoto. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo panali itapita miyezi itatu, anamuuza Yuda kuti, Tamara mpongozi wako wachita chigololo, ndiponso taonani, ali ndi pakati ndi chigololocho. Ndipo Yuda anati, Mtulutse iye kuti amponye pamoto. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Patapita miyezi itatu, munthu wina adauza Yuda kuti, “Mpongozi wanu uja Tamara adachita chigololo, ndipo ali ndi pathupi.” Pomwepo Yuda adalamula kuti, “Kamtengeni ndipo mukamtenthe kuti afe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Patapita miyezi itatu, Yuda anawuzidwa kuti, “Mpongozi wanu Tamara anachita zadama, ndipo zotsatira zake nʼzakuti ali ndi pathupi.” Yuda anati, “Kamutulutseni ndipo mukamutenthe kuti afe!” Onani mutuwo |