Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 38:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo mkazi anauka nachoka, navula chofunda chake, navala zovala zamasiye zake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo mkazi anauka nachoka, navula chofunda chake, navala zovala zamasiye zake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Tsono Tamara adanyamuka nachokapo. Adachotsa nsalu imene adaadziphimba nayo kumaso ija, navalanso zovala zake zaumasiye zija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Kenaka Tamara anachoka, navula nsalu anadziphimba nayo ija, navalanso zovala zake za umasiye zija.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 38:19
5 Mawu Ofanana  

Pamenepo anavula zovala zake zamasiye, nadzifunda ndi chofunda chake, navala nakhala pa chipata cha Enaimu, chifukwa chili panjira ya ku Timna; pakuti anaona kuti Sela anakula msinkhu, ndipo sanampatse iye kuti akhale mkazi wake.


Ndipo iye anati, Chikole chanji ndidzakupatsa iwe? Ndipo mkazi anati, Mphete yako, ndi chingwe chako, ndi ndodo ili m'dzanja lako. Ndipo anampatsa izo, nalowana naye, ndipo mkazi anatenga pakati ndi iye.


Ndipo Yuda anatumiza kamwana kambuzi ndi dzanja la bwenzi lake Mwadulamu, kuti alandire chikole padzanja la mkazi; koma sanampeze iye.


Ndipo Yowabu anatumiza ku Tekowa, natenga kumeneko mkazi wanzeru, nanena naye, Ukokomezeke monga mfedwa, nuvale zovala za pamaliro, osadzola mafuta, koma ukhale ngati munthu wamkazi wakulira akufa nthawi yaikulu.


Ndipo mfumuyo inanena naye, Usowanji? Iye nayankha, Zoonadi ine ndine mkazi wamasiye, mwamuna wanga anamwalira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa