Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 37:30 - Buku Lopatulika

30 Ndipo anabwera kwa abale ake, nati, Mwana palibe; ndipo ine ndipita kuti?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndipo anabwera kwa abale ake, nati, Mwana palibe; ndipo ine ndipita kuti?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Ndipo adabwerera kwa abale ake aja naŵauza kuti, “Mnyamata ujatu palibe! Tsono ine ndichite chiyani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 nabwerera kwa abale ake nati, “Mnyamata uja mulibemo! Nanga ndilowere kuti ine tsopano?”

Onani mutuwo Koperani




Genesis 37:30
5 Mawu Ofanana  

Tiyeni tsopano timuphe iye timponye m'dzenje, ndipo tidzati, Wajiwa ndi chilombo; ndipo tidzaona momwe adzachita maloto ake.


Nati iwo, Akapolo anu ndife abale khumi, ana aamuna a munthu mmodzi m'dziko la Kanani; ndipo, taonani, wamng'ono ali ndi atate wathu lero; ndipo palibe mmodzi.


tili abale khumi ndi awiri, ana a atate wathu; wina palibe, ndipo lero wamng'ono ali ndi atate wathu m'dziko la Kanani.


Atero Yehova: Mau a amveka mu Rama, maliro ndi kulira kwakuwawa, Rakele alinkulirira ana ake; akana kutonthozedwa mtima pa ana ake, chifukwa palibe iwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa