Genesis 37:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo Yuda anati kwa abale ake, Nanga tidzapindulanji tikamupha mbale wathu ndi kufotsera mwazi wake? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo Yuda anati kwa abale ake, Nanga tidzapindulanji tikamupha mbale wathu ndi kufotsera mwazi wake? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Tsono Yuda adafunsa abale ake kuti, “Kodi tipindulanji tikamupha mbale wathuyu ndi kubisa, osaulula kuti tamupha? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Yuda anafunsa abale ake nati, “Kodi tidzapindula chiyani tikapha mʼbale wathuyu ndi kuphimbitsa magazi ake? Onani mutuwo |