Genesis 37:27 - Buku Lopatulika27 Tiyeni timgulitse iye kwa Aismaele, tisasamulire iye manja; chifukwa ndiye mbale wathu, thupi lathu. Ndipo anamvera iye abale ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Tiyeni timgulitse iye kwa Aismaele, tisasamulire iye manja; chifukwa ndiye mbale wathu, thupi lathu. Ndipo anamvera iye abale ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Tiyeni timgulitse kwa Aismaeleŵa. Nanga iyeyu si mbale wathu, thupi limodzi ndiponso magazi amodzi?” Abale akewo adavomereza zimenezo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Bwanji timugulitse kwa Aismaeliwa, koma ife tisamuchite kanthu kalikonse. Ameneyu ndi mʼbale wathu thupi limodzi ndi ife.” Abale ake anavomereza zimenezi. Onani mutuwo |