Genesis 37:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Yakobo anakhala m'dziko limene anakhalamo mlendo atate wake, m'dziko la Kanani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Yakobo anakhala m'dziko limene anakhalamo mlendo atate wake, m'dziko la Kanani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Yakobe adakhalabe ku dziko la Kanani kumene bambo wake ankakhala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yakobo ankakhala mʼdziko la Kanaani kumene abambo ake ankakhala. Onani mutuwo |