Genesis 36:13 - Buku Lopatulika13 Ndi ana aamuna a Reuwele: Nahati, ndi Zera, Sama, ndi Miza; amenewa ndi ana a Basemati mkazi wake wa Esau. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndi ana amuna a Reuwele: Nahati, ndi Zera, Sama, ndi Miza; amenewa ndi ana a Basemati mkazi wake wa Esau. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ana a Reuele ndi aŵa: Nahati, Zera, Sama ndi Miza. Ameneŵa ndiwo ana a Basemati mkazi wa Esau. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Awa ndi ana a Reueli: Nahati, Zera, Sama ndi Miza. Amenewa ndi ana a Basemati, mkazi wa Esau. Onani mutuwo |