Genesis 32:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo kudamchera iye pamene anaoloka pa Penuwele, ndipo iye anatsimphina ndi ntchafu yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo kudamchera iye pamene anaoloka pa Penuwele, ndipo iye anatsimphina ndi ntchafu yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Dzuŵa lidamtulukira Yakobe pamene ankachoka ku Penuwele, ndipo ankayenda chotsimphina chifukwa cha nyung'unyu ija. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Dzuwa linamutulukira Yakobo pamene amachoka pa Penueli. Tsono ankayenda chotsimphina chifukwa cha nyungʼunyu yake ija. Onani mutuwo |