Genesis 32:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo Yakobo anatcha dzina la malo amenewo, Penuwele: chifukwa ndaonana ndi Mulungu nkhope ndi nkhope, ndipo wapulumuka moyo wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo Yakobo anatcha dzina la malo amenewo, Penuwele: chifukwa ndaonana ndi Mulungu nkhope ndi nkhope, ndipo wapulumuka moyo wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Yakobe adati, “Ndamuwona Mulungu maso ndi maso, ndipo ndili moyobe.” Tsono malowo adaŵatcha Penuwele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Choncho Yakobo anawatcha malowo Penueli, popeza anati, “Ndinaonana ndi Mulungu maso ndi maso koma sindinafe.” Onani mutuwo |